LyricsCrawler: The lyrics spot for those who know how to spot a spot.
Home Search Contact Us

Artists:  # A B C D E F G H I J K L M N O P Q R S T U V W X Y Z

Google
Web Lyricscrawler.com
Unknown Lyrics - Malawi Native Anthem Text

1.
Mlungu dalitsani Malawi,
Mumsunge m'mtendere.
Gonjetsani adani onse,
Njala, nthenda, nsanje.
Lunzitsani mitima yathu,
Kuti tisaope.
Mdalitse Mtsogo leri na fe,
Ndi Mai Malawi.
2.
Malawi ndziko lokongola,
La chonde ndi ufulu,
Nyanja ndi mphepo ya m'mapiri,
Ndithudi tadala.
Zigwa, mapiri, nthaka, dzinthu,
N'mphatso zaulere.
Nkhalango, madambo abwino.
Ngwokoma Malawi.
3.
O! Ufulu tigwirizane,
Kukweza Malawi.
Ndi chikondi, khama, kumvera,
Timutumikire.
Pa nkhondo nkana pa mtendere,
Cholinga n'chimodzi.
Mai, bambo, tidzipereke,
Pokweza Malawi.
Sent by Carlos André Pereira da Silva Branco

Artists:  # A B C D E F G H I J K L M N O P Q R S T U V W X Y Z

All lyrics are property and copyright of their respective owners.
All lyrics are provided for educational purposes only and contributed by users.
All the Rest © 2003-2005 Roy Russo. All rights reserved.

Our Privacy Policy  ::  Contact
WorldofQuotes.com :: CheatsCrawler.com

Page Generated in: 0.020802021026611 seconds.